Job 6:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma abwenzi anga ndi onyenga, ngati mtsinje wothamanga, ngati mitsinje youma msanga mvula ikasoŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Abale anga anachita monyenga ngati kamtsinje, ngati madzi a timitsinje akupitirira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma abale anga ndi wosadalirika ngati mitsinje yowuma msanga, ngati mitsinje imene imathamanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Abale anga anacita monyenga ngati kamtsinje, Ngati madzi a timitsinje akupitirira.