Job 6:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ali ngati mitsinje ya madzi abii nthaŵi ya dzinja, imene madzi ake amakhala ambiri chifukwa cha kuchuluka kwa mvula.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amada chifukwa cha madzi oundana. M'menemo chipale chofewa chibisika;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ali ngati mitsinje ya madzi akuda nthawi ya dzinja, imene madzi ake amakhala ambiri chifukwa chakuchuluka kwa mvula,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amada cifukwa ca madzi oundana. M'menemo cipale cofewa cibisika;