Job 6:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma pa nthaŵi ya mafundi imauma, kukatentha imamwerera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
atafikira mafundi, mitsinje iuma; kukatentha, imwerera m'malo mwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
koma madziwo amasiya kuyenda nthawi yachilimwe, ndipo nthawi yotentha madziwo amawumiratu mʼmitsinjemo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atafikira mafundi, mitsinje iuma; Kukatentha, imwerera m'malo mwao.