Job 6:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Oyenda pa ngamira a ku Tema amaifunafuna mitsinjeyo. Alendo a ku Sheba amaidalira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Aulendo a ku Tema anapenyerera, makamu a ku Sheba anaiyembekezera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu oyenda pa ngamira a ku Tema amafunafuna madzi, anthu amalonda apaulendo a ku Seba amafunafuna mwa chiyembekezo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Aulendo a ku Tema anapenyerera, Makamu a ku Seba anaiyembekezera.