Job 6:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amataya mtima chifukwa ankayembekeza kupeza madzi, koma pofika kumeneko, angoti kakasi, poti idauma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anazimidwa popeza adaikhulupirira; anafikako, nathedwa nzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amataya mtima chifukwa ankayembekezera kupeza madzi; koma akafika kumeneko, amangokhumudwako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anazimidwa popeza adaikhulupirira; Anafikako, nathedwa nzeru.