Job 6:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi ndanena kuti, ‘Mundipatse mphatso,’ kapena kuti, ‘Mupereke chiphuphu kwa wina chifukwa cha ine?’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati ndinati, Mundipatse? Kapena, Muperekeko kwa ine chuma chanu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ine ndinanenapo kuti, ‘Ndiperekereni kenakake, ndilipirireni dipo kuchokera pa chuma chanu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati ndinati, Mundipatse? Kapena, Muperekeko kwa ine cuma canu?