Job 6:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi inu mukufuna kundidzudzuliranji? Monga simukuwona kuti mau a munthu wotaya mtima ndi mphepo chabe?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi muyesa kudzudzula mau? Popeza maneno a munthu wodololoka akunga mphepo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi inu mukufuna kundidzudzula pa zimene ndikunena, ndipo mukufuna kuyesa mawu a munthu wosweka mtima ngati mphepo chabe?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi muyesa kudzudzula mau? Popeza maneno a munthu wodololoka akunga mphepo.