Job 6:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
bwenzi atalemera kupambana mchenga wonse wam'nyanja. Nchifukwa chake kulankhula kwanga kuli kokadzulira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti zikadalemera tsopano koposa mchenga wa kunyanja; chifukwa chake mau anga ndasonthokera kunena.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndithu, zikanalemera kupambana mchenga wa ku nyanja; nʼchifukwa chake mawu anga akhala okhadzula.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti zikadalemera tsopano koposa mcenga wa kunyanja; Cifukwa cace mau anga ndasonthokera kunena.