Job 6:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi mukuganiza kuti ndikulankhula zabodza? Monga ine sindingasiyanitse chabwino ndi choipa?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi pali chosalungama palilime panga? Ngati sindizindikira zopanda pake m'kamwa mwanga?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi pali choyipa chilichonse pa milomo yanga? Kodi pakamwa panga sipangathe kuzindikira kanthu koyipa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi pali cosalungama palilime panga? Ngati sindizindikira zopanda pace m'kamwa mwanga?