Job 6:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoonadi mivi yake ya Mphambe yandibaya, thupi langa likumva ululu wa miviyo. Zoopsa za Mulungu zandizinga, kuti zilimbane nane.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti mivi ya Wamphamvuyonse yandilowa, mzimu wanga uwumwa ulembe wake; zoopsa za Mulungu zindindandira nkhondo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mivi ya Wamphamvuzonse yandibaya, thupi langa likumva ululu wa miviyo; zoopsa za Mulungu zandizinga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti mibvi ya Wamphamvuyonse yandilowa, Mzimu wanga uumwa ulembe wace; Zoopsa za Mulungu zindindandira nkhondo.