Job 6:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zakudya zimenezi sindifuna nkuzilaŵa komwe, zakudya zake ndi zobwerera kukhosi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zimene moyo wanga ukana kuzikhudza zikunga chakudya chosakolera kwa ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zakudya zimenezi sindifuna nʼkuzilawa komwe; zakudya zimenezi zimabwerera kukhosi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zimene moyo wanga ukana kuzikhudza Zikunga cakudya cosakolera kwa ine.