Job 7:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikagona pansi kuti ndithuze mtima, ndi kupeza mpumulo pabedi panga,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikati, Pakama panga mpondisangalatsa, pogona panga padzachepsa chondidandaulitsa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene ndikuganiza kuti ndidzapeza chitonthozo pa bedi panga ndipo pogona panga padzachepetsa madandawulo anga,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikati, Pakama panga mpondisangalatsa, Pogona panga padzacepsa condidandaulitsa;