Job 7:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho ndikadasankha kudzikhweza kapena kufa kumene, kupambana kupirira zovuta zimene ndikuzimva m'thupi mwanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
potero moyo wanga usankha kupotedwa, ndi imfa, koposa mafupa anga awa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kotero kuti ndimalakalaka kudzikhweza kapena kufa, kupambana kupirira zowawa zimene ndikuzimva mʼthupi mwanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero moyo wanga usankha kupotedwa, Ndi imfa, koposa mafupa anga awa.