Job 7:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Mulungu, kodi munthu nchiyani, kuti muzimganizira chotere, kuti muzisamala zochita zake?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu ndani kuti mumkuze, ndi kuti muike mtima wanu pa iye,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi munthu nʼchiyani kuti muzimuganizira chotere, kuti muzisamala zochita zake,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu ndani kuti mumkuze, Ndi kuti muike mtima wanu pa iye,