Job 7:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mumampenyetsetsa masiku onse, ndipo mumamuyesa nthaŵi zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kuti mucheze naye m'mawa ndi m'mawa, ndi kumuyesa nthawi zonse?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuti muzimusanthula mmawa uliwonse ndi kumamuyesa nthawi yonse?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi kuti muceze naye m'mawa ndi m'mawa, Ndi kumuyesa nthawi zonse?