Job 7:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Masiku anga ndi othamanga kupambana makina oombera nsalu, amatha opanda chikhulupiriro chilichonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Masiku anga afulumira koposa mphindo ya muomba, apitirira opanda chiyembekezo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Masiku anga ndi othamanga kupambana makina wolukira nsalu, ndipo amatha wopanda chiyembekezo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Masiku anga afulumira koposa mphindo ya muomba, Apitirira opanda ciyembekezo.