Job 8:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mizu yake imayanga pa miyala, ndipo imakangamira pa thanthwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mizu yake iyangayanga pa kasupe wamadzi, apenyerera pokhalapo miyala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mizu yake imayanga pa mulu wa miyala ndi kufunafuna malo woti izikike pa miyalapo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mizu yace iyangayanga pa kasupe wamadzi, Apenyerera pokhalapo miyala.