Joel 2:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Masiku amenewo, ndidzatsitsa mzimu wanga ngakhale pa akapolo ndi pa adzakazi omwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi pa akapolo ndi adzakazi omwe ndidzatsanulira mzimu wanga masiku awo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhalenso pa antchito anga aamuna ndi aakazi ndidzakhuthulira Mzimu wanga masiku amenewo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi pa akapolo ndi adzakazi omwe ndidzatsanulira mzimu wanga masiku awo.