John 1:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuchokera m'kukoma mtima kwake kwathunthu ife tonse tidalandira madalitso, madalitso ake otsatanatsatana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa mwa kudzala kwake tinalandira ife tonse, chisomo chosinthana ndi chisomo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuchokera mʼkuchuluka kwa chisomo chake ife tonse talandira madalitso pamwamba pa madalitso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa mwa kudzala kwace tinalandira ife tonse, cisomo cosinthana ndi cisomo.