John 1:36 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene adaona Yesu akuyenda, iye adati, “Suuyu Mwanawankhosa wa Mulungu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo poyang'ana Yesu alikuyenda, anati, Onani Mwanawankhosa wa Mulungu!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye ataona Yesu akudutsa anati, “Taonani Mwana Wankhosa wa Mulungu!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo poyang'ana Yesu alikuyenda, anati, 10 Onani Mwanawankhosa wa Mulungu!