John 1:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuŵalako kukuunikabe mu mdima, ndipo mdima sudathe kugonjetsa kuŵalako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kuunikaku kunawala mumdima; ndi mdimawu sunakuzindikira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuwunika kunawala mu mdima, koma mdimawo sunakuzindikire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kuunikaku kunawala mumdima; ndi mdimawu sunakuzindikira.