John 1:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sikuti iyeyo ndiye anali kuŵalako ai, koma adangobwera kudzachitira umboni kuŵalako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye sindiye kuunikaku, koma anatumidwa kukachita umboni wa kuunikaku.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iyeyu sanali kuwunika; koma anabwera ngati mboni ya kuwunika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
iye sindiye kuunikaku, koma anatumidwa kukacita umboni wa kuunikaku.