John 10:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wolembedwa ntchito uja amathaŵa, chifukwa amangotsata malipiro chabe, ndipo salabadirako za nkhosazo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chifukwa ali wolipidwa, ndipo sasamala nkhosa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthuyo amathawa chifukwa ndi wantchito ndipo sasamalira chilichonse cha nkhosazo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
cifukwa ali wolipidwa, ndipo sasamala nkhosa.