John 11:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene Yesu adafika ku Betaniya, adapeza Lazaro atagona m'manda masiku anai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene Yesu anadza, anapeza kuti pamenepo atakhala m'manda masiku anai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu atafika, anapeza kuti Lazaro anali atagona mʼmanda masiku anayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene Yesu anadza, anapeza kuti pamenepo atakhala m'manda masiku anai.