John 11:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo nkuti Yesu asanafike kumudziko, koma anali chikhalire pamalo pomwe Marita adaakumana naye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
(Koma Yesu sanafike kumudzi, koma anali pamalo pomwe Marita adakomana ndi Iye.)
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsopano nʼkuti Yesu asanalowe mʼmudzi, koma anali akanali pa malo pamene Marita anakumana naye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
(Koma Yesu sanafike kumudzi, koma anali pamalo pomwe Marita adakomana ndi Iye)