John 11:46 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ena adapita kwa Afarisi, nakaŵasimbira zimene Yesu adaachita.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ena a mwa iwo anamuka kwa Afarisi, nawauza zimene Yesu adazichita.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ena a iwo anapita kwa Afarisi ndi kukawawuza zimene Yesu anachita.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ena a mwa iwo anamuka kwa Afarisi, nawauza zimene Yesu adazicita.