John 11:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye kuti Yesu ankakonda Marita ndi mng'ono wake Maria ndiponso Lazaro.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Yesu anakonda Marita, ndi mbale wake, ndi Lazaro.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anakonda Marita, mchemwali wake ndi Lazaro.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Yesu anakonda Marita, ndi mbale wace, ndi Lazaro.