John 12:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaŵauza kuti, “Mauŵa amveka osati chifukwa cha Ine ai, koma chifukwa cha inu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu anayankha nati, Mau awa sanafika chifukwa cha Ine, koma cha inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anati, “Mawu awa abwera chifukwa cha inu osati chifukwa cha Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu anayankha nati, Mau awa sanafika cifukwa ca Ine, koma ca inu.