John 12:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo Ine, akadzandipachika, ndidzakokera anthu onse kwa Ine.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Ine, m'mene ndikakwezedwa kudziko, ndidzakoka anthu onse kwa Ine ndekha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Ine, akadzandipachika pa dziko lapansi, ndidzakokera anthu onse kwa Ine.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Ine, m'mene ndikakwezedwa kudziko, ndidzakoka anthu onse kwa Ine ndekha.