John 12:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
(Adaanena mau ameneŵa kuti aŵadziŵitse za m'mene analikudzafera.)
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ananena ichi ndi kuzindikiritsa imfa yanji akuti adzafa nayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye ananena izi kuti aonetse mmene adzafere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ananena ici ndi kuzindikiritsa imfa yanji akuti adzafa nayo.