John 13:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wophunzira wina, yemwe Yesu ankamukonda kwambiri, adaakhala pambali pa Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mmodzi wa ophunzira ake, amene Yesu anamkonda, analikutsamira pa chifuwa cha Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mmodzi wa ophunzira ake amene Yesu anamukonda, anali atatsamira pachifuwa chake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mmodzi wa akuphunzira ace, amene Yesu anamkonda, analikutsamira pa cifuwa ca Yesu.