John 13:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu ankadziŵa kuti Atate adapereka zinthu zonse m'manja mwake. Ankadziŵanso kuti adachokera kwa Mulungu, ndipo kuti akubwerera kwa Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu, podziwa kuti Atate adampatsa Iye zonse m'manja mwake, ndi kuti anachokera kwa Mulungu, namuka kwa Mulungu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu podziwa kuti Atate anamupatsa Iye zonse mʼmanja mwake, ndi kuti Iye anachokera kwa Mulungu ndipo amabwerera kwa Mulunguyo;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu, podziwa kuti Atate adampatsa iye zonse m'manja mwace, ndi kuti anacokera kwa Mulungu, namuka kwa Mulungu,