John 15:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate anga ndi mlimi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate wanga ndiye wam'munda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate anga ndiye mwini munda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate wanga ndiye wam'munda.