John 15:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngati anthu odalira zapansipano adana nanu, kumbukirani kuti adadana ndi Ine asanadane nanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati dziko lapansi lida inu, mudziwa kuti lidada Ine lisanayambe kuda inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ngati dziko lapansi lidana nanu, dziwani kuti linayamba kudana ndi Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati dziko lapansi lida inu, mudziwa kuti lidada Ine lisanayambe kuda inu.