John 15:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu mwayera kale chifukwa cha mau amene ndakuuzani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwakhala okonzeka tsopano inu chifukwa cha mau amene ndalankhula ndi inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu ndinu oyera kale chifukwa cha mawu amene ndayankhula inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwakhala okonzeka tsopano inu cifukwa ca mau amene ndalankhula ndi inu,