John 16:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngolakwa pa za kulungama, chifukwa ndikupita kwa Atate ndipo simudzandiwonanso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
za chilungamo, chifukwa ndinka kwa Atate, ndipo simundionanso;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Za chilungamo, chifukwa Ine ndi kupita kwa Atate, kumene simudzandionanso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
za cilungamo, cifukwa ndinka kwa Atate, ndipo simundionanso;