John 16:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndili nawo mau ena ambiri oti ndikuuzeni, koma simungathe kuŵamvetsa tsopano ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndili nazo zambirinso zakunena kwa inu, koma simungathe kuzisenza tsopano lino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine ndili ndi zambiri zoti ndiyankhule nanu, koma simungathe kuzilandira tsopano.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiri nazo zambirinso zakunena kwa inu, koma simungathe kuzisenza tsopano lino.