John 16:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku limenelo mudzapempha potchula dzina langa, ndipo sindikuti Ine ndidzakupempherani kwa Atate ai,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsiku limenelo mudzapempha m'dzina langa; ndipo sindinena kwa inu kuti Ine ndidzafunsira inu kwa Atate;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsiku limenelo inu mudzapempha mʼdzina langa. Ine sindikunena kuti ndidzapempha Atate mʼmalo mwanu ayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsiku limenelo mudzapempha m'dzina langa; ndipo sindinena kwa inu kuti Ine ndidzafunsira inu kwa Atate;