John 16:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'mitima mwanu mwadzaza chisoni chifukwa ndakuuzani zimenezi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma chifukwa ndalankhula izi ndi inu chisoni chadzala mumtima mwanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Muli ndi chisoni kwambiri chifukwa ndakuwuzani zimene.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma cifukwa ndalankhula izi ndi inu cisoni cadzala mumtima mwanu.