John 16:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngolakwa pa za kuchimwa, chifukwa sandikhulupirira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
za machimo, chifukwa sakhulupirira Ine;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Za uchimo, chifukwa anthu sakhulupirira Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
za macimo, cifukwa sakhulupirira Ine;