John 17:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Amene mudaŵapatula mwa anthu onse ndi kundipatsa Ine, ndaŵadziŵitsa dzina lanu. Anali anu, Inu mudaŵapereka kwa Ine, ndipo adasunga mau anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndalionetsera dzina lanu kwa anthu amene mwandipatsa Ine m'dziko lapansi; anali anu, ndipo mwandipatsa Ine iwo; ndipo adasunga mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine ndawadziwitsa za Inu anthu amene munandipatsa mʼdziko lapansi. Iwo anali anu. Inu munawapereka kwa Ine ndipo amvera mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndalionetsera dzina lanu kwa anthu amene mwandipatsa Ine m'dziko lapansi; anali anu, ndipo mwandipatsa Ine iwo; ndipo adasunga mau anu.