John 18:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Petro adaima pa khomo kunja. Wophunzira wina uja, amene anali wodziŵikayo, adatuluka nakalankhula ndi mtsikana wolonda pa khomo, nkumuloŵetsa Petroyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma Petro anaima kukhomo kunja. Chifukwa chake wophunzira winayo amene anadziwika kwa mkulu wa ansembe, anatuluka nalankhula ndi wapakhomo, nalowetsa Petro.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
koma Petro anadikira kunja pa khomo. Ophunzira winayo amene amadziwika kwa mkulu wa ansembe, anatuluka ndi kuyankhula ndi mtsikana amene anali mlonda wa pa khomo ndi kumulowetsa Petro.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma Petro anaima kukhomo kunja, Cifukwa cace wophunzira winayo amene anadziwika kwa mkulu wa ansembe, anaturuka nalankhula ndi wapakhomo, nalowetsa Petro.