John 18:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adati, “Ine ndinkalankhula mosabisa pamaso pa anthu onse. Ndinkaphunzitsa m'nyumba zamapemphero ndiponso m'Nyumba ya Mulungu, m'mene anthu onse amasonkhana. Sindidalankhule kanthu mobisa ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu anayankha iye, Ine ndalankhula zomveka kwa dziko lapansi; ndinaphunzitsa Ine nthawi zonse m'sunagoge ndi m'Kachisi, kumene amasonkhana Ayuda onse; ndipo mobisika sindinalankhula kanthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anayankha kuti, “Ine ndinayankhula poyera ku dziko lapansi. Nthawi zonse ndimaphunzitsa mʼsunagoge kapena mʼNyumba ya Mulungu kumene Ayuda onse amasonkhana pamodzi. Ine sindimanena kanthu mseri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu anayankha iye, Ine ndalankhula zomveka kwa dziko lapansi; ndinaphunzitsa Ine nthawi zonse m'sunagoge ndi m'Kacisi, kumene amasonkhana Ayuda onse; ndipo mobisika sindinalankhula kanthu.