John 18:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atanena zimenezi, mmodzi mwa asilikali oimirira pomwepo adamenya Yesu kumaso, adati, “Ungayankhe choncho kwa mkulu wa ansembe onse?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma m'mene Iye adanena izi, mmodzi wa anyamata akuimirirako anapanda Yesu khofu, ndi kuti, Kodi uyankha mkulu wa ansembe chomwecho?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu atanena izi, mmodzi wa akuluakulu amene anali pafupi anamumenya kumaso. Iye anafunsa kuti, “Mayankhidwe awa ndi woti ndi kuyankha mkulu wa ansembe?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma m'mene iye adanena izi, mmodzi wa anyamata akuimirirako anapanda Yesu khofu, ndi kuti, Kodi uyankha mkulu wa ansembe comweco?