John 18:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho Pilato adaŵauza kuti, “Mtengenitu tsono inuyo, mukamuweruze potsata malamulo anu.” Koma Ayudawo adati, “Ife sitiloledwa kupha munthu ai.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Pilato anati kwa iwo, Mumtenge Iye inu, ndi kumweruza Iye monga mwa chilamulo chanu. Ayuda anati kwa iye, Tilibe ulamuliro wakupha munthu aliyense;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pilato anati, “Mutengeni inu eni ake ndi kumuweruza Iye monga mwa malamulo anu.” Ayuda anatsutsa nati, “Koma tilibe ulamuliro wakupha aliyense.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Pilato anati kwa iwo, Mumtenge iye inu, ndi kumweruza iye monga mwa cilamulo canu. Ayuda anati kwa iye, Tiribe ulamuliro wakupha munthu ali yense;