John 18:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
(Zidaatero kuti zipherezere zimene Yesu adaanena za imfa yake.)
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti mau a Yesu akwaniridwe, amene ananena akuzindikiritsa imfa imene akuti adzafa nayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Izi zinachitika kuti mawu a Yesu amene anayankhula kusonyeza mtundu wa imfa imene Iye anati adzafe nayo akwaniritsidwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti mau a Yesu akwaniridwe, amene ananena akuzindikiritsa imfa imene, akuti adzafa nayo.