John 18:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pilato adaloŵanso m'nyumba yake ija, naitana Yesu. Adamufunsa kuti, “Kodi iwe, ndiwe Mfumu ya Ayuda?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake Pilato analowanso m'Pretorio, naitana Yesu, nati kwa Iye, Iwe ndiwe mfumu ya Ayuda kodi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka Pilato anapita mʼkati mwa nyumba yaufumu nayitanitsa Yesu, ndipo anamufunsa kuti, “Kodi iwe ndi mfumu ya Ayuda?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace Pilato analowanso m'Pretorio, naitana Yesu, nati kwa iye, Iwe ndiwe Mfumu ya Ayuda kodi?