John 18:34 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adati, “Kodi mukunena zimenezi mwa inu nokha, kapena ena adakuuzani za Ine?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu anayankha, Kodi munena ichi mwa inu nokha, kapena ena anakuuzani za Ine?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anafunsa kuti, “Kodi amenewo ndi maganizo anu wokha? Kapena kuti ena anakuwuzani za Ine?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu anayankha, Kodi munena ici mwa inu nokha, kapena ena anakuuzani za Ine?