John 18:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene Yesu adaŵayankha kuti, “Ndine, ndilipo,” iwo adabwerera m'mbuyo nagwa pansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Yesu anati, “Ndine,” iwo anabwerera mʼmbuyo ndi kugwa pansi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi.