John 18:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaŵafunsanso kuti, “Mukufuna yani kodi?” Iwo aja adati “Tikufuna Yesu wa ku Nazarete.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anawafunsanso kuti, “Kodi mukumufuna ndani?” Ndipo iwo anati, “Yesu wa ku Nazareti.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? koma iwo anati, Yesu Mnazarayo.